The value of a soul - Part 3 (CHICHEWA)

SERMON TOPIC: The value of a soul - Part 3 (CHICHEWA)

Speaker: Gavin Paynter

Language: CHICHEWA

Date: 30 March 2015

Topic Groups:

Sermon synopsis: Q: Kodi moyo wanu ndi wa mtengo wapatali bwanji kwa inu?

A: Moyo wanu ndiye chuma choposa chuma chirichonse chimene mungathe kukhala nacho.

Moyo uposa thupi:

Mateyu 10:28 Ndipo musamaopa amene akupha thupi, koma moyo sangathe kuupha.

Moyo uli wa mtengo wake wapatali kuposa chuma chonse cha dziko lapansi:

Mateyu 16:26 Pakuti munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekenji chosintha ndi moyo wake?
- Download notes (6.06 MB, 1632 downloads)

- Download audio (7.75 MB, 1272 downloads)
- All sermons by Gavin Paynter

- All sermons in CHICHEWA




IP:Country:City:Region: