The value of a soul - Part 3 (CHICHEWA)
SERMON TOPIC: The value of a soul - Part 3 (CHICHEWA)
Speaker: Gavin Paynter
Language: CHICHEWA
Date: 30 March 2015
Topic Groups:
Sermon synopsis: Q: Kodi moyo wanu ndi wa mtengo wapatali bwanji kwa inu?
A: Moyo wanu ndiye chuma choposa chuma chirichonse chimene mungathe kukhala nacho.
Moyo uposa thupi:
Mateyu 10:28 Ndipo musamaopa amene akupha thupi, koma moyo sangathe kuupha.
Moyo uli wa mtengo wake wapatali kuposa chuma chonse cha dziko lapansi:
Mateyu 16:26 Pakuti munthu adzapindulanji akalandira dziko lonse lapansi nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekenji chosintha ndi moyo wake?
IP:Country:City:Region:
|