Sermon No: 2601-The book of lifeSERMON TOPIC: The book of lifeSpeaker: Gavin PaynterLanguage: CHICHEWA Date: 15 February 2015Topic Groups: Sermon synopsis: Mneneri wa Mulungu Mose adanena kuti Mulungu ali Ndi Buku la kulembamo:
Eksodo 32:32 “… Ngati mukana mundifafanizetu, kundichotsatu mbuku lanu limene munalembera.”
Mtumwi Yohane ali kunenana kuti Buku lotchedwa “Buku la moyo”Ndilo la Mwana wa nkhosa( Yesu)
Chibvumbulutso 13:8 …Mbuku lamoyo la mwana wa nkhosa wophedwa kuyambira makhazikidwe adziko lapansi. IP:Country:City:Region: |