The book of life

SERMON TOPIC: The book of life

Speaker: Gavin Paynter

Language: CHICHEWA

Date: 15 February 2015

Topic Groups:

Sermon synopsis: Mneneri wa Mulungu Mose adanena kuti Mulungu ali Ndi Buku la kulembamo:
Eksodo 32:32 “… Ngati mukana mundifafanizetu, kundichotsatu mbuku lanu limene munalembera.”
Mtumwi Yohane ali kunenana kuti Buku lotchedwa “Buku la moyo”Ndilo la Mwana wa nkhosa( Yesu)
Chibvumbulutso 13:8 …Mbuku lamoyo la mwana wa nkhosa wophedwa kuyambira makhazikidwe adziko lapansi.
- Download notes (1.42 MB, 1476 downloads)

- All sermons by Gavin Paynter

- All sermons in CHICHEWA




IP:Country:City:Region: