TSIKU-LA-ADAMBO

SERMON TOPIC: TSIKU-LA-ADAMBO

Speaker: Gavin Paynter

Language: CHICHEWA

Date: 13 July 2017

Topic Groups:

Sermon synopsis: 1 Yohane 2:13 Ndikulemberani atate popeza mwamzindikira Iye, amene ali kuyambira pachiyambi.
Ndikulemberani anyamata popeza mwamulaka oyipayo, ndikulemberani ana popeza mwazindikira Atate.

Yohane analemba mosiyanitsa mitundu itatu ya akhristu:
1) Ana
2) Anyamata
3) Atate
Kodi kusiyana kwawo kuli pati?

1) Ana – Amasowa wina awayang’anire.
2) Anyamata – amadziyang’anira okha.
3) Atate – Samangodziyang’anira okha komanso amayang’aniranso anthu ena.
“Atate” ngakhalenso amayi sachita kubadwa, anyamata amakula kukhala abambo pamene atsikana amakula kukhala amayi. Izi adalankhula ndi bambo - David M. Gottesman


- Download notes (1.33 MB, 836 downloads)

- All sermons by Gavin Paynter

- All sermons in CHICHEWA




IP:Country:City:Region: