TSIKU-LA-ADAMBO
SERMON TOPIC: TSIKU-LA-ADAMBO
Speaker: Gavin Paynter
Language: CHICHEWA
Date: 13 July 2017
Topic Groups:
Sermon synopsis: 1 Yohane 2:13 Ndikulemberani atate popeza mwamzindikira Iye, amene ali kuyambira pachiyambi. Ndikulemberani anyamata popeza mwamulaka oyipayo, ndikulemberani ana popeza mwazindikira Atate. Yohane analemba mosiyanitsa mitundu itatu ya akhristu: 1) Ana 2) Anyamata 3) Atate Kodi kusiyana kwawo kuli pati? 1) Ana – Amasowa wina awayang’anire. 2) Anyamata – amadziyang’anira okha. 3) Atate – Samangodziyang’anira okha komanso amayang’aniranso anthu ena. “Atate” ngakhalenso amayi sachita kubadwa, anyamata amakula kukhala abambo pamene atsikana amakula kukhala amayi. Izi adalankhula ndi bambo - David M. Gottesman
IP:Country:City:Region:
|