The cares of this life - CHICHEWA
SERMON TOPIC: The cares of this life - CHICHEWA
Speaker: Ken Paynter
Language: CHICHEWA
Date: 5 April 2014
Topic Groups:
Sermon synopsis: KODI MWAPSINJIKA NDINKHAWA ZA MOYO UNO? MULUNGU AKUTI MUMUTULIRE IYE. 1 PETRO 5:6-7 Potero dzichepetseni pansi pa dzanja la mphamvu la Mulungu, kuti pantawi yache akukwezeni;ndi kutaya pa iye nkhawa yanu yonse, pakuti iye asamalira inu. MAU A MULUNGU AMATIUZA KUTI NJIRA YABWINO YOMWE TINGAONETSERE KUDZICHEPETSA, NDIYO POMWE TISANKHA KUTULA NKHAWA ZATHU PA MULUNGU. “TAYANI NKHAWA ZANU ZONSE” PA IYE – TKUZINDIKIRA KOMANSO KUVOMEREZA KUTI PA WEKHA SUNGAKWANITSE KUPEZA NJIRA PA WEKHA YOTHANIRANA NDI NKHAWA ZAKO.
IP:Country:City:Region:
|